Ndiwe Wanga lyrics by Maskal - original song full text. Official Ndiwe Wanga lyrics, 2024 version | LyricsMode.com
Request & respond explanations
  • Don't understand the meaning of the song?
  • Highlight lyrics and request an explanation.
  • Click on highlighted lyrics to explain.
Maskal – Ndiwe Wanga lyrics
Verse; 1
Pazachikondi chako dziwa ine ndi mboni
Sindinalakelake kupita ku Joni
Chikondi cha iwe ndi ine sicham'mafoni
Nchifukwa sindinapite ku bank kukatenga loan
Chikondi chathu chobeba chanoninoni
Umandizula moyo ukapereka moni
Umandikumbutsa za kwathu kumangoni
Ndakondwa umadziwa kuti ine ndi m'goni

Chorus*2
Ndiwe wanga ndiwe kuwala kwanga
Ndiwe wanga ndiwe nyenyezi yanga
Ndiwe wanga ndiwe wanga ndiwe wapamtima wanga
Ndiwe wanga ndiwe wanga nyenyezi yanga
Ndiwe wanga ndiwe kuwala kwanga

Verse; 2
Ndikakha pansi ndimadziwa ndiri ndi mzanga
Kuyenda limodzi tifanana mawanga
Amandinena ati ndiri nyanga
Asatilongoze monga ichita nkhanga
Ndithudi ndilonjeza ndzakutengela kunyanja
Nthawi imeneyo tikukonzekera banja
Ona ambiri akutiombera m'manja
Mpakana wena kutimangira nsanja

(Back to chorus)

Verse; 3
Chikondi chathu chansangala sizachisoni
Ena amasangalala akatipatsa moni
Unasiya amabenzi onse ndimalinkoni
Amatithila madzi ndikumaimba horn
Akamadutsa baby, Samamvetsa baby
Ngati andale baby, Ali pa njale baby
Zimawawawa baby, Kuiwala mawa baby
Ngati moyenda baby, Ife tikuyenda baby!, Hee!

(Back to chorus till the end)
×



Lyrics taken from /lyrics/m/maskal/ndiwe_wanga.html

  • Email
  • Correct
Submitted by Maskal

Ndiwe Wanga meanings

Write about your feelings and thoughts about Ndiwe Wanga

Know what this song is about? Does it mean anything special hidden between the lines to you? Share your meaning with community, make it interesting and valuable. Make sure you've read our simple tips.
U
Min 50 words
Not bad
Good
Awesome!

Post meanings

U
Min 50 words
Not bad
Good
Awesome!

official video

Featured lyrics

0-9 A B C D E F G H I J K L M N O P Q R S T U V W X Y Z